Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Zekariya 8:1 - Buku Lopatulika

Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta Wamphamvuzonse adandipatsanso uthenga uwu wakuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Awa ndi mawu amene Yehova Wamphamvuzonse ananena.

Onani mutuwo



Zekariya 8:1
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, ndi kuti,


koma ndidzawabalalitsa ndi kamvulumvulu mwa amitundu onse amene sanawadziwe. Motero dziko linakhala bwinja, m'mbuyo mwao; palibe munthu wopitapo ndi kubwererako; pakuti adaika dziko lofunikalo labwinja.


Atero Yehova wa makamu: Ndimchitira nsanje Ziyoni ndi nsanje yaikulu, ndipo ndimchitira nsanje ndi ukali waukulu.