Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Zekariya 7:8 - Buku Lopatulika

Ndipo mau a Yehova anadza kwa Zekariya, ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mau a Yehova anadza kwa Zekariya, ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adapatsa Zekariya uthenga uwu wakuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Yehova anayankhulanso ndi Zekariya kuti,

Onani mutuwo



Zekariya 7:8
4 Mawu Ofanana  

sitinamvere atumiki anu aneneri, amene ananena m'dzina lanu kwa mafumu athu, akalonga athu, makolo athu, ndi anthu onse a m'dziko.


Pamene Mose adamva ichi chidamkomera pamaso pake.


Si ndiwo mau Yehova anawalalikira mwa aneneri oyamba aja, muja Yerusalemu anali nao okhalamo, ndi wokhazikika; ndi m'mizinda mwake pozungulira pake, ndi m'dziko la kumwera, ndi m'chidikha munali anthu okhalamo?


Watero Yehova wa makamu, kuti, Weruzani chiweruzo choona, nimuchitire yense mnzake chifundo ndi ukoma mtima;