Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Zekariya 7:4 - Buku Lopatulika

Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Chauta Wamphamvuzonse adandipatsa uthenga uwu wakuti:

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo Yehova Wamphamvuzonse anayankhula nane kuti,

Onani mutuwo



Zekariya 7:4
3 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake Ambuye, Yehova wa makamu, adzatumiza kuonda mwa onenepa ake; ndipo pansi pa ulemerero wake padzayaka kutentha, konga ngati kutentha kwa moto.


nanene kwa ansembe a nyumba ya Yehova wa makamu, ndi kwa aneneri, ndi kuti, Kodi ndilire mwezi wachisanu, ndi kudzipatula, monga umo ndikachitira zaka izi zambiri?


Nena kwa anthu onse a m'dziko, ndi kwa ansembe, kuti, Muja mukasala ndi kulira mwezi wachisanu, ndi wachisanu ndi chitatu, zaka izi makumi asanu ndi awiri, kodi mukasalira Ine, Inedi?