Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Zekariya 6:9 - Buku Lopatulika

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kenaka Chauta adandipatsa uthenga wakuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anayankhula nane kuti,

Onani mutuwo



Zekariya 6:9
3 Mawu Ofanana  

Mwezi wachisanu ndi chitatu, chaka chachiwiri cha Dariusi, mau a Yehova anadza kwa Zekariya mwana wa Berekiya, mwana wa Ido mneneri, ndi kuti,


Ndipo kunachitika chaka chachinai cha mfumu Dariusi, mau a Yehova anadza kwa Zekariya tsiku lachinai la mwezi wachisanu ndi chinai, ndiwo Kisilevi.


Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,