Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Zekariya 6:2 - Buku Lopatulika

Ku galeta woyamba kunali akavalo ofiira; ndi kugaleta wachiwiri akavalo akuda;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ku galeta woyamba kunali akavalo ofiira; ndi kugaleta wachiwiri akavalo akuda;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Galeta loyamba linkakokedwa ndi akavalo ofiira, lachiŵiri akavalo akuda,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Galeta loyamba limakokedwa ndi akavalo ofiira, lachiwiri ndi akavalo akuda,

Onani mutuwo



Zekariya 6:2
5 Mawu Ofanana  

Ndinaona usiku, taonani, munthu woyenda pa kavalo wofiira, alikuima pakati pa mitengo yamchisu inali kunsi; ndi pambuyo pake panali akavalo ofiira, odera ndi oyera.


Galeta wa akavalo akuda atulukira kudziko la kumpoto; ndi oyerawo atulukira kuwatsata; ndi amawanga atulukira kudziko la kumwera.


Ndipo chinaoneka chizindikiro china m'mwamba taonani, chinjoka chofiira, chachikulu, chakukhala nayo mitu isanu ndi iwiri, ndi nyanga khumi, ndi pamutu pake nduwira zachifumu zisanu ndi ziwiri.


Ndipo ananditenga kunka nane kuchipululu, mu Mzimu; ndipo ndinaona mkazi alinkukhala pachilombo chofiira, chodzala ndi maina a mwano, chakukhala nayo mitu isanu ndi iwiri ndi nyanga khumi.