Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Zekariya 3:6 - Buku Lopatulika

Ndipo mthenga wa Yehova anamchitira Yoswa umboni, ndi kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mthenga wa Yehova anamchitira Yoswa umboni, ndi kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mngelo wa Chauta uja adauza Yoswa kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mngelo wa Yehova analimbikitsa Yoswa kuti,

Onani mutuwo



Zekariya 3:6
11 Mawu Ofanana  

M'mazunzo ao onse Iye anazunzidwa, ndipo mthenga wakuimirira pamaso pake anawapulumutsa; m'kukonda kwake ndi m'chisoni chake Iye anawaombola, nawabereka nawanyamula masiku onse akale.


Pakuti ndinatsimikizitsa kwa atate anu tsiku lomwe ndinawatulutsa iwo kudziko la Ejipito, mpaka lero lomwe, kuuka mamawa ndi kutsimikiza, kuti, Mverani mau anga.


inde, analimbana ndi wamthenga nampambana; analira, nampembedza Iye; anampeza Iye ku Betele, ndi kumeneko Iye analankhula ndi ife;


Pamenepo anandionetsa Yoswa mkulu wa ansembe alikuima pamaso pa mthenga wa Yehova, ndi Satana alikuima padzanja lake lamanja, atsutsana naye.


Ndipo ndinati, Amuike nduwira yoyera pamutu pake. Naika nduwira yoyera pamutu pake, namveka ndi zovala; ndi mthenga wa Yehova anaimirirapo.


Atero Yehova wa makamu: Ukadzayenda m'njira zanga, ndi kusunga udikiro wanga, pamenepo udzaweruza nyumba yanga, ndi kusunga mabwalo anga, ndipo ndidzakupatsa malo oyendamo mwa awa oimirirapo.