Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Zefaniya 2:12 - Buku Lopatulika

Inunso Akusi, mudzaphedwa ndi lupanga langa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Inunso Akusi, mudzaphedwa ndi lupanga langa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inunso Aetiopiya, Chauta adzakukanthani ndi lupanga lake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Inunso anthu a ku Kusi, mudzaphedwa ndi lupanga.”

Onani mutuwo



Zefaniya 2:12
12 Mawu Ofanana  

Ukani Yehova, Mumtsekereze, mumgwetse, landitsani moyo wanga kwa woipa ndi lupanga lanu;


Iwe Asiriya chibonga cha mkwiyo wanga, ndodo m'dzanja lake muli ukali wanga!


Achokera m'dziko lakutali, kumalekezero a thambo, ngakhale Yehova, ndi zida za mkwiyo wake, kuti aononge dziko lonse.


Ndipo Yehova anati, Monga mtumiki wanga Yesaya wayenda maliseche ndi wopanda nsapato zaka zitatu, akhale chizindikiro ndi chodabwitsa kwa Ejipito ndi kwa Etiopiya;


Chifukwa kuti Ine ndine Yehova Mulungu wako, Woyera wa Israele, Mpulumutsi wako; ndapatsa Ejipito dombolo lako, Etiopiya ndi Seba m'malo mwako.


Ndipo ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babiloni, ndi kuika lupanga langa m'dzanja lake; koma ndidzathyola manja a Farao, ndipo adzabuula pamaso pake mabuulo a munthu wopyozedwa.