Zefaniya 1:5 - Buku Lopatulika
ndi iwo akulambira khamu la kumwamba pamwamba pa matsindwi; ndi iwo akulambira, akulumbira pali Yehova, nalumbiranso pali mfumu;
Onani mutuwo
ndi iwo akulambira khamu la kumwamba pamwamba pa matsindwi; ndi iwo akulambira, akulumbira pali Yehova, nalumbiranso pali mfumu;
Onani mutuwo
Ndidzafafanizanso amene amaŵerama pa madenga ao nkumapembedza dzuŵa, mwezi ndi nyenyezi. Ndidzaononganso amene amati kwinaku akulambira Chauta ndi kulumbira m'dzina lake, kwinaku nkumalumbira m'dzina la Milikomu.
Onani mutuwo
amene amagwada pa madenga a nyumba zawo kupembedza zolengedwa zamumlengalenga, amene amagwada ndi kulumbira mʼdzina la Yehova, komanso mʼdzina la Moleki,
Onani mutuwo