Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yoweli 3:20 - Buku Lopatulika

Koma Yuda adzakhala chikhalire, ndi Yerusalemu ku mibadwomibadwo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Yuda adzakhala chikhalire, ndi Yerusalemu ku mibadwomibadwo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma ku Yudako kudzakhala anthu mpaka muyaya, ndipo ku Yerusalemu sikudzatha anthu pa mibadwo yonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Yuda adzakhala ndi anthu mpaka muyaya ndi Yerusalemu ku mibadomibado.

Onani mutuwo



Yoweli 3:20
3 Mawu Ofanana  

Tayang'ana pa Ziyoni, mzinda wa zikondwerero zathu; maso ako adzaona, Yerusalemu malo a phee, chihema chimene sichidzasunthidwa, zichiri zake sizidzazulidwa konse, zingwe zake sizidzadulidwa.


Ndipo adzakhala m'dziko ndinalipereka kwa Yakobo mtumiki wanga, limene anakhalamo makolo anu, ndipo adzakhala m'mwemo iwo, ndi ana ao, ndi zidzukulu zao kosatha; ndi Davide mtumiki wanga adzakhala mtsogoleri wao kosatha.


Ndipo ndidzawaoka m'dziko mwao ndipo sadzazulidwanso m'dziko lao limene ndawapatsa, ati Yehova Mulungu wako.