Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yoweli 1:17 - Buku Lopatulika

Mbeu zaola pansi pa zibuluma zao; zosungiramo zaonongeka, nkhokwe zapasuka; pakuti tirigu wakwinyata.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mbeu zaola pansi pa zibuluma zao; zosungiramo zaonongeka, nkhokwe zapasuka; pakuti tirigu wakwinyata.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mbeu zakongonyala, poti pansi mpouma. Nyumba zosungiramo dzinthu zaonongeka, nkhokwe zapasuka, popeza kuti zokolola palibe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mbewu zikunyala poti pansi ndi powuma. Nyumba zosungiramo zinthu zawonongeka; nkhokwe zapasuka popeza tirigu wauma.

Onani mutuwo



Yoweli 1:17
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anamvera Efuroni, ndipo Abrahamu anamuyesera Efuroni ndalama zimene ananena alinkumva ana a Hiti, masekeli a siliva mazana anai, ndalama zomwezo agulana nazo malonda.


Yang'anirani mbalame za kumwamba, kuti sizimafesa ai, kapena sizimatema ai, kapena sizimatutira m'nkhokwe; ndipo Atate wanu wa Kumwamba azidyetsa. Nanga inu mulibe kusiyana nazo kuziposa kodi?