Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yoswa 1:3 - Buku Lopatulika

Pali ponse phazi lanu lidzapondapo ndinakupatsani, monga ndinanena ndi Mose.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pali ponse phazi lanu lidzapondapo ndinakupatsani, monga ndinanena ndi Mose.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Paliponse pamene muponde phazi lanu, ndakupatsani inu, monga momwe ndidalonjezera Mose.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Paliponse pamene phazi lanu liponde, ndikupatsani monga momwe ndinalonjezera Mose.

Onani mutuwo



Yoswa 1:3
4 Mawu Ofanana  

Pamalo ponse padzapondapo phazi lanu ndi panu, kuyambira chipululu ndi Lebanoni, kuyambira pamtsinjewo, mtsinje wa Yufurate, kufikira nyanja ya m'tsogolo, ndiwo malire anu.


m'chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu, wosanamayo, analonjeza zisanayambe nthawi zosayamba;


Kuyambira chipululu, ndi Lebanoni uyu, kufikira mtsinje waukulu mtsinje wa Yufurate, dziko lonse la Ahiti, ndi kufikira Nyanja Yaikulu ku malowero a dzuwa, ndiwo malire anu.


Ndipo Mose analumbira tsiku lomwelo ndi kuti, Zedi, dzikoli phazi lako lapondapo lidzakhala cholowa chako, ndi cha ana ako kosalekeza, chifukwa unatsata Yehova Mulungu wanga ndi mtima wonse.