Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yona 2:3 - Buku Lopatulika

Pakuti munandiponya mwakuya m'kati mwa nyanja, ndipo madzi anandizinga; mafunde anu onse a nyondonyondo anandimiza.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti munandiponya mwakuya m'kati mwa nyanja, ndipo madzi anandizinga; mafunde anu onse a nyondonyondo anandimiza.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mudandiponya m'nyanja yozama, m'kati mwenimweni mwa njanja, ndipo mweza wam'nyanjamo udandizungulira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munandiponya mʼnyanja yozama, mʼkati mwenimweni mwa nyanja, ndipo madzi oyenda anandizungulira; mafunde anu onse ndi mkokomo wake zinandimiza.

Onani mutuwo



Yona 2:3
11 Mawu Ofanana  

Pakuti mafunde a imfa anandizinga, mitsinje ya zopanda pake inandiopsa ine.


Ndimkonda, popeza Yehova amamva mau anga ndi kupemba kwanga.


Popeza amanditcherera khutu lake, chifukwa chake ndidzaitanira Iye masiku anga onse.


Ndinafuulira kwa Yehova mu msauko wanga, ndipo anandivomereza.


Madzi akuya aitanizana ndi madzi akuya, pa mkokomo wa matiti anu; mafunde onse a nyondonyondo anandimiza ine.


madzi anayenda pamwamba pamutu panga, ndinati, Ndalikhidwa.


Ndinaitana dzina lanu, Yehova, ndili m'dzenje lapansi;