Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 9:9 - Buku Lopatulika

Ena ananena, kuti, Ndiyeyu; ena ananena, Iai, koma afanana naye. Iyeyu anati, Ndine amene.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ena ananena, kuti, Ndiyeyu; ena ananena, Iai, koma afanana naye. Iyeyu anati, Ndine amene.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ena adati, “Ndiye amene.” Ena nkumati, “Iyai, akungofanafana naye.” Koma mwiniwakeyo adati, “Ai ndithu, ndine amene.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ena ananena kuti anali yemweyo. Ena anati, “Ayi, sakuoneka ngati yemweyo.” Koma iye mwini ananenetsa kuti, “Munthuyo ndine.”

Onani mutuwo



Yohane 9:9
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo anenana ndi iye, Nanga maso ako anatseguka bwanji?


Chifukwa chake anzake ndi iwo adamuona kale, kuti anali wopemphapempha, ananena, Kodi si uyu uja wokhala ndi kupemphapempha?