Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 9:6 - Buku Lopatulika

Pamene ananena izi, analavula pansi, nakanda thope ndi malovuwo, napaka thopelo m'maso,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamene ananena izi, analavula pansi, nakanda thope ndi malovuwo, napaka thopelo m'maso,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atanena zimenezi, Yesu adalavulira malovu pansi, nakanda thope ndi malovuwo. Kenaka adapaka thopelo m'maso mwa munthuyo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atanena izi, Iye anathira malovu pansi ndi kukanda dothi, napaka matopewo mʼmaso a munthuyo.

Onani mutuwo



Yohane 9:6
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo maso a akhungu adzatsegudwa, ndi makutu a ogontha adzatsegulidwa.


Ndipo anampatula pa khamu la anthu pa yekha, nalonga zala zake m'makutu mwake, nalavula malovu, nakhudza lilime lake:


Ndipo anamgwira dzanja munthu wakhunguyo, natulukira naye kunja kwa mudzi; ndipo atamthira malovu m'maso mwake, naika manja pa iye, anamfunsa, Uona kanthu kodi?


Iyeyu anayankha, Munthuyo wotchedwa Yesu anakanda thope, napaka m'maso mwanga, nati, kwa ine, Muka ku Siloamu kasambe; chifukwa chake ndinachoka, ndipo m'mene ndinasamba ndinapenya.


ndikulangiza ugule kwa Ine golide woyengeka m'moto, kuti ukakhale wachuma, ndi zovala zoyera, kuti ukadziveke, ndi kuti manyazi a usiwa wako asaoneke; ndi mankhwala opaka m'maso mwako, kuti ukaone.