Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 9:14 - Buku Lopatulika

Koma tsikulo ndi la Sabata limene Yesu anakanda thope, namtsegulira iye maso ake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma tsikulo ndi la Sabata limene Yesu anakanda thope, namtsegulira iye maso ake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsiku limene Yesu adaakanda thope namchiritsalo linali la Sabata.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono linali la Sabata tsiku limene Yesu anakanda dothi ndi kutsekula maso a munthuyu.

Onani mutuwo



Yohane 9:14
11 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali kuti anapita Iye pakati pa minda tsiku la Sabata; ndipo ophunzira ake poyenda anayamba kubudula ngala za dzinthu.


Ndipo panali pamene Iye analowa m'nyumba ya mmodzi wa akulu a Afarisi tsiku la Sabata, kukadya, iwo analikumzonda Iye.


Ndipo chifukwa cha ichi Ayuda analondalonda Yesu, popeza anachita izo tsiku la Sabata.


Ndipo pomwepo munthuyu anachira, nayalula mphasa yake, nayenda. Koma tsiku lomwelo linali la Sabata.


Anapita naye amene anali wosaona kale kwa Afarisi.


Pamene ananena izi, analavula pansi, nakanda thope ndi malovuwo, napaka thopelo m'maso,