Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 9:13 - Buku Lopatulika

Anapita naye amene anali wosaona kale kwa Afarisi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anapita naye amene anali wosaona kale kwa Afarisi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono munthu uja kale sankapenyayu adapita naye kwa Afarisi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anabwera naye munthu amene poyamba anali wosaona kwa Afarisi.

Onani mutuwo



Yohane 9:13
7 Mawu Ofanana  

Koma ansembe aakulu ndi Afarisi adalamula kuti, munthu wina akadziwa pokhala Iye, aulule, kuti akamgwire Iye.


Chifukwa chake Afarisi ananena wina ndi mnzake, Muona kuti simupindula kanthu konse; onani dziko litsata pambuyo pake pa Iye.


Kungakhale kotero, ambiri a mwa akulu anakhulupirira Iye; koma chifukwa cha Afarisi sanavomereze, kuti angaletsedwe m'sunagoge,


Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.


Koma tsikulo ndi la Sabata limene Yesu anakanda thope, namtsegulira iye maso ake.