Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 9:12 - Buku Lopatulika

Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthuwo adamufunsa kuti, “Iyeyo ali kuti?” Munthu uja adati, “Kaya, sindikudziŵa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anamufunsa iye kuti, “Ali kuti munthu ameneyu?” Iye anati, “Ine sindikudziwa.”

Onani mutuwo



Yohane 9:12
5 Mawu Ofanana  

Pomwepo Ayuda analikumfuna Iye pachikondwerero, nanena, Ali kuti uja?


Iyeyu anayankha, Munthuyo wotchedwa Yesu anakanda thope, napaka m'maso mwanga, nati, kwa ine, Muka ku Siloamu kasambe; chifukwa chake ndinachoka, ndipo m'mene ndinasamba ndinapenya.


Anapita naye amene anali wosaona kale kwa Afarisi.