Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 8:45 - Buku Lopatulika

Koma Ine, chifukwa ndinena choonadi, simukhulupirira Ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Ine, chifukwa ndinena choonadi, simukhulupirira Ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Ine ndimalankhula zoona, nchifukwa chake simundikhulupirira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma chifukwa ndikuwuzani choonadi, inu simukundikhulupirira Ine!

Onani mutuwo



Yohane 8:45
7 Mawu Ofanana  

Pamenepo Pilato anati kwa Iye, Nanga kodi ndiwe Mfumu? Yesu anayankha, Munena kuti ndine Mfumu. Ndinabadwira ichi Ine, ndipo ndinadzera ichi kudza kudziko lapansi, kuti ndikachite umboni ndi choonadi. Yense wakukhala mwa choonadi amva mau anga.


Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa.


Ndani mwa inu anditsutsa Ine za tchimo? Ngati ndinena choonadi, simundikhulupirira Ine chifukwa ninji?


Kotero kodi ndasanduka mdani wanu, pakukunenerani zoona?


ndi m'chinyengo chonse cha chosalungama kwa iwo akuonongeka, popeza chikondi cha choonadi sanachilandire, kuti akapulumutsidwe iwo.