Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 8:30 - Buku Lopatulika

Pakulankhula Iye zimenezi ambiri anakhulupirira Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakulankhula Iye zimenezi ambiri anakhulupirira Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Yesu ankalankhula zimenezi, anthu ambiri adamkhulupirira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Iye ankayankhula zimenezi, ambiri anamukhulupirira.

Onani mutuwo



Yohane 8:30
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ambiri anakhulupirira Iye komweko.


Chifukwa chake ambiri a mwa Ayuda amene anadza kwa Maria, m'mene anaona chimene anachita, anakhulupirira Iye.


Koma pamene anali mu Yerusalemu pa Paska pachikondwerero, ambiri anakhulupirira dzina lake, pakuona zizindikiro zake zimene anachitazi.


Chifukwa chake, anthu, poona chizindikiro chimene anachita, ananena, kuti, Ameneyo ndiye mneneri ndithu wakudzayo m'dziko lapansi.


Koma ambiri a m'khamu la anthu anakhulupirira Iye; ndipo ananena, Pamene Khristu akadza kodi adzachita zizindikiro zambiri zoposa zimene adazichita ameneyo?