Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 8:13 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake Afarisi anati kwa Iye, Muchita umboni wa Inu nokha; umboni wanu suli woona.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake Afarisi anati kwa Iye, Muchita umboni wa Inu nokha; umboni wanu suli woona.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Afarisi adamuuza kuti, “Ukudzichitira wekha umboni. Umboni wakowo ngwosakwanira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Afarisi anamutsutsa Iye nati, “Iwe ukudzichitira umboni wa Iwe mwini, umboni wako siwoona.”

Onani mutuwo



Yohane 8:13
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anamkulunga Iye m'maso, namfunsa, nati, Talota; anakupanda Iwe ndani?