Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:47 - Buku Lopatulika

Pamenepo Afarisi anayankha iwo, Kodi mwasokeretsedwa inunso?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Afarisi anayankha iwo, Kodi mwasokeretsedwa inunso?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Afarisi adati, “Kani inunso wakunyengani?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Afarisi anawadzudzula nati, “Kodi mukutanthauza kuti Iye anakunamizani inunso?”

Onani mutuwo



Yohane 7:47
8 Mawu Ofanana  

Itero mfumu, Asakunyengeni Hezekiya; pakuti sadzakhoza kukulanditsani m'dzanja lake;


mpaka ndifika ndi kumuka nanu ku dziko lakunga dziko lanu, dziko la tirigu ndi vinyo, dziko la mkate ndi minda yampesa, dziko la azitona ndi la uchi; kuti mukhale ndi moyo osafai; nimusamvere Hezekiya akakukopani, ndi kuti, Yehova adzatilanditsa.


Ndipo tsono, asakunyengeni Hezekiya, ndi kukukopani motero, musamkhulupirira; pakuti palibe Mulungu wa mtundu uliwonse wa anthu, kapena ufumu uliwonse, unakhoza kulanditsa anthu ake m'dzanja mwanga; ndipo kodi Mulungu wanu adzakulanditsani inu m'dzanja langa?


Ndipo Iye anayankha, nati kwa iwo, Inunso mulumphiranji lamulo la Mulungu chifukwa cha miyambo yanu?


nanena, Mfumu, takumbukira ife kuti wonyenga uja anati, pamene anali ndi moyo, Ndidzauka pofika masiku atatu.


Ndipo kunali kung'ung'udza kwambiri za Iye m'makamu a anthu; ena ananena, kuti, Ali wabwino; koma ena ananena, Iai, koma asocheretsa khamu la anthuwo.


mwa ulemerero, mwa mnyozo, mwa mbiri yoipa ndi mbiri yabwino; monga osocheretsa, angakhale ali oona;