Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:44 - Buku Lopatulika

Koma ena mwa iwo anafuna kumgwira Iye; koma palibe munthu anamgwira kumanja.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ena mwa iwo anafuna kumgwira Iye; koma palibe munthu anamgwira kumanja.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ena ankafuna kumgwira, koma panalibe amene adamkhudza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ena anafuna kumugwira Iye, koma palibe amene anayika dzanja pa Iye.

Onani mutuwo



Yohane 7:44
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Afarisi anatuluka, nakhala upo womchitira Iye mwa kumuononga.


Pamenepo anafuna kumgwira Iye; koma palibe wina anamgwira kumanja, chifukwa nthawi yake siinafike.


Mau awa analankhula m'nyumba yosungiramo chuma cha Mulungu pophunzitsa mu Kachisi; ndipo palibe munthu anamgwira Iye, pakuti nthawi yake siinafike.


chifukwa Ine ndili pamodzi ndi iwe, ndipo palibe munthu adzautsana ndi iwe kuti akuipse; chifukwa ndili nao anthu ambiri m'mzinda muno.


Ndipo usiku wake Ambuye anaimirira pa iye, nati, Limbika mtima; pakuti monga wandichitira umboni ku Yerusalemu, koteronso uyenera kundichitira umboni ku Roma.