Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:40 - Buku Lopatulika

Pamenepo ena a khamulo pakumva mau awa, ananena, Mneneriyo ndi uyu ndithu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo ena a khamulo pakumva mau awa, ananena, Mneneriyo ndi uyu ndithu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene khamu la anthu lidamva mau ameneŵa, ena mwa iwo ankati, “Zoonadi munthuyu ndiye Mneneri uja.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakumva mawu ake, ena a anthuwo anati, “Zoonadi munthu uyu ndi mneneri.”

Onani mutuwo



Yohane 7:40
6 Mawu Ofanana  

Ndipo makamu a anthu anati, Uyu ndi mneneri Yesu wa ku Nazarete wa ku Galileya.


Ndipo anamfunsa iye, Nanga bwanji? Ndiwe Eliya kodi? Nanena iye, Sindine iye. Ndiwe Mneneriyo kodi? Nayankha, Iai.


Mkazi ananena ndi Iye, Ambuye, ndizindikira kuti muli Mneneri.


Chifukwa chake, anthu, poona chizindikiro chimene anachita, ananena, kuti, Ameneyo ndiye mneneri ndithu wakudzayo m'dziko lapansi.


Ndipo kunali kung'ung'udza kwambiri za Iye m'makamu a anthu; ena ananena, kuti, Ali wabwino; koma ena ananena, Iai, koma asocheretsa khamu la anthuwo.