Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:24 - Buku Lopatulika

Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Musamaweruza poyang'ana maonekedwe chabe, koma muziweruza molungama.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Musamaweruze potengera maonekedwe chabe, koma weruzani molungama.”

Onani mutuwo



Yohane 7:24
17 Mawu Ofanana  

Mudzaweruza mosalunjika kufikira liti, ndi kusamalira nkhope ya oipa?


Wokometsa mlandu wa wamphulupulu, ndi wotsutsa wolungama, onse awiriwa amnyansa Yehova.


Izinso zili za anzeru, poweruza chetera silili labwino.


amene alungamitsa woipa pa chokometsera mlandu, nachotsera wolungama chilungamo chake!


Musamachita chisalungamo pakuweruza mlandu; usamavomereza munthu wosauka, kapena kulemekeza munthu womveka; uweruze mlandu wa munthu mnzako molungama.


Watero Yehova wa makamu, kuti, Weruzani chiweruzo choona, nimuchitire yense mnzake chifundo ndi ukoma mtima;


Pamenepo ena a iwo a ku Yerusalemu ananena, Kodi suyu amene afuna kumupha?


Inu muweruza monga mwa thupi; Ine sindiweruza munthu.


Kodi mupenyera zopenyeka pamaso? Ngati wina alimbika mwa yekha kuti ali wa Khristu, ayesere ichinso mwa iye yekha, kuti monga iye ali wa Khristu, koteronso ife.


Abale anga, pakuti muli nacho chikhulupiriro cha Ambuye wathu Yesu Khristu, Ambuye wa ulemerero, musakhale okondera ndi kusamala maonekedwe.


kodi simunasiyanitse mwa inu nokha, ndi kukhala oweruza oganizira zoipa?


koma ngati musamala maonekedwe, muchita uchimo, ndipo mutsutsidwa ndi chilamulo monga olakwa.