Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:21 - Buku Lopatulika

Yesu anayankha nati kwa iwo, Ndinachita ntchito imodzi, ndipo muzizwa monse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu anayankha nati kwa iwo, Ndinachita ntchito imodzi, ndipo muzizwa monse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adati, “Ndinangochita ntchito yozizwitsa imodzi yokha, nonsenu nkumadabwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anawawuza kuti, “Ine ndinachita chodabwitsa chimodzi ndipo inu mwadabwa.

Onani mutuwo



Yohane 7:21
3 Mawu Ofanana  

Ndipo chifukwa cha ichi Ayuda analondalonda Yesu, popeza anachita izo tsiku la Sabata.


Ngati munthu alandira mdulidwe tsiku la Sabata, kuti chilamulo cha Mose chingapasulidwe; kodi mundikwiyira Ine, chifukwa ndamchiritsadi munthu tsiku la Sabata?