Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 6:8 - Buku Lopatulika

Mmodzi wa ophunzira ake, Andrea, mbale wake wa Simoni Petro, ananena ndi Iye,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mmodzi wa ophunzira ake, Andrea, mbale wake wa Simoni Petro, ananena ndi Iye,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Wophunzira wake wina, dzina lake Andrea, mbale wake wa Simoni Petro, adauza Yesu kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mmodzi wa ophunzira ake, Andreya, mʼbale wa Simoni Petro, anati,

Onani mutuwo



Yohane 6:8
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Yesu analikuyenda m'mbali mwa nyanja ya Galileya, anaona abale awiri, Simoni wonenedwa Petro, ndi Andrea, mbale wake, analikuponya khoka m'nyanja; popeza anali asodzi a nsomba.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.