Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 6:34 - Buku Lopatulika

Pamenepo anati kwa Iye, Ambuye, tipatseni ife mkate umene nthawi zonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo anati kwa Iye, Ambuye, tipatseni ife mkate umene nthawi zonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo anthuwo adapempha Yesu kuti, “Ambuye, muzitipatsa chakudya chimenecho masiku onse.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anati, “Ambuye, kuyambira tsopano muzitipatsa buledi ameneyu.”

Onani mutuwo



Yohane 6:34
4 Mawu Ofanana  

Ambiri amati, Adzationetsa chabwino ndani? Weramutsirani ife kuunika kwa nkhope yanu, Yehova.


Mkaziyo ananena kwa Iye, Ambuye, ndipatseni madzi amene, kuti ndisamve ludzu, kapena ndisadze kuno kudzatunga.


Yesu anayankha iwo nati, Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Mundifuna Ine, si chifukwa munaona zizindikiro, koma chifukwa munadya mkate, nimunakhuta.


Mulungu Atate wa Ambuye Yesu, Iye amene alemekezeka kunthawi yonse, adziwa kuti sindinama.