Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 6:18 - Buku Lopatulika

Ndipo nyanja inalikuuka chifukwa cha mphepo yaikulu yakuombako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo nyanja inalikuuka chifukwa cha mphepo yaikulu yakuombako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komanso nyanja idaavwanduka, chifukwa mphepo inkaomba kwambiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mphepo yamphamvu inawomba ndipo nyanja inalusa.

Onani mutuwo



Yohane 6:18
5 Mawu Ofanana  

Popeza anena, nautsa namondwe, amene autsa mafunde ake.


Akweza mitambo ichokere ku malekezero a dziko lapansi; ang'animitsa mphezi zidzetse mvula; atulutsa mphepo mosungira mwake.


Koma pomwepo ngalawa idafika pakati pa nyanja, yozunzika ndi mafunde; pakuti mphepo inadza mokomana nao.


ndipo pamene adalowa m'ngalawa, analikuoloka nyanja kunka ku Kapernao. Ndipo kutada pamenepo, koma Yesu asanadze kwa iwo.


Ndipo pamene adapalasa monga mastadiya makumi awiri ndi asanu kapena makumi atatu, anaona Yesu alikuyenda panyanja, ndi kuyandikira ngalawa; ndipo anachita mantha.