Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 6:13 - Buku Lopatulika

Pomwepo anasonkhanitsa, nadzaza madengu khumi ndi awiri ndi makombo a mikate isanuyo yabarele, amene anatsalira anadyawo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pomwepo anasonkhanitsa, nadzaza madengu khumi ndi awiri ndi makombo a mikate isanuyo yabarele, amene anatsalira anadyawo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adatoladi zotsala zonse za buledi msanu uja, nadzaza madengu khumi ndi aŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho iwo anasonkhanitsa makombo nadzaza madengu khumi ndi awiri.

Onani mutuwo



Yohane 6:13
9 Mawu Ofanana  

Potero anawagawira, nadya, nasiyapo, monga mwa mau a Yehova.


Ndipo Amaziya anati kwa munthu wa Mulungu, Koma nanga titani nao matalente zana limodzi ndinapatsa ankhondo a Israele? Nati munthu wa Mulungu, Yehova ali nazo zoposa izi kukupatsani.


Ndipo anadya onse, nakhuta; ndipo anatola makombo otsala, nadzala madengu khumi ndi iwiri.


Pali mnyamata pano, amene ali nayo mikate isanu yabarele, ndi tinsomba tiwiri; koma nanga izi zikwanira bwanji ambiri otere?


Koma Mulungu wanga adzakwaniritsa chosowa chanu chilichonse monga mwa chuma chake mu ulemerero mwa Khristu Yesu.