Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 6:10 - Buku Lopatulika

Nati Yesu, Akhalitseni anthu pansi. Ndipo panali udzu wambiri pamalopo. Pamenepo amunawo anakhala pansi, kuwerenga kwao monga zikwi zisanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nati Yesu, Akhalitseni anthu pansi. Ndipo panali udzu wambiri pamalopo. Pamenepo amunawo anakhala pansi, kuwerenga kwao monga zikwi zisanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adati, “Auzeni anthu akhale pansi.” (Pamenepo panali msipu wambiri.) Anthuwo adakhaladi pansi. Amuna okha analipo ngati zikwi zisanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anati, “Awuzeni anthuwa akhale pansi.” Pamalo pamenepa panali udzu wambiri ndipo amuna amene anakhala pansi anali osachepera 5,000.

Onani mutuwo



Yohane 6:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anadyawo anali amuna monga zikwi zisanu, kuwaleka akazi ndi ana.