Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 5:47 - Buku Lopatulika

Koma ngati simukhulupirira malembo a iyeyu, mudzakhulupirira bwanji mau anga?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ngati simukhulupirira malembo a iyeyu, mudzakhulupirira bwanji mau anga?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma ngati simukhulupirira zimene iyeyo adalemba, nanga mungakhulupirire bwanji mau anga?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma ngati simukhulupirira zimene iye analemba, mudzakhulupirira bwanji zimene Ine ndikunena?”

Onani mutuwo



Yohane 5:47
3 Mawu Ofanana  

Koma Abrahamu anati, Ali ndi Mose ndi aneneri; amvere iwo.


Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa.


ndi kuti kuyambira ukhanda wako wadziwa malembo opatulika, okhoza kukupatsa nzeru kufikira chipulumutso, mwa chikhulupiriro cha mwa Khristu Yesu.