Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 5:41 - Buku Lopatulika

Ulemu sindiulandira kwa anthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ulemu sindiulandira kwa anthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Sindikufunafuna ulemu wa anthu ai.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ine sindilandira ulemu kuchokera kwa anthu

Onani mutuwo



Yohane 5:41
12 Mawu Ofanana  

pakuti anakonda ulemerero wa anthu koposa ulemerero wa Mulungu.


Ndipo Ine sindilandira umboni kwa munthu: koma ndinena izi, kuti inu mukapulumutsidwe.


ndipo simufuna kudza kwa Ine, kuti mukhale nao moyo.


Koma ndikudziwani inu, kuti mulibe chikondi cha Mulungu mwa inu nokha.


Mungathe inu bwanji kukhulupirira, popeza mulandira ulemu wina kwa mnzake ndipo ulemu wakuchokera kwa Mulungu yekha simuufuna?


Pamenepo Yesu, pozindikira kuti alikufuna kudza kudzamgwira Iye, kuti amlonge ufumu, anachokanso kunka kuphiri pa yekha.


Iye wolankhula zochokera kwa iye yekha afuna ulemu wa mwini yekha. Iye wakufuna ulemu wa Iye amene anamtuma, yemweyu ali woona, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama.


Koma Ine sinditsata ulemerero wanga; alipo woutsata ndi wakuweruza.


Yesu anayankha, Ngati Ine ndidzilemekeza ndekha, ulemerero wanga uli chabe; Atate wanga ndiye wondilemekeza Ine; amene munena za Iye, kuti ndiye Mulungu wanu;


kapena sitinakhale ofuna ulemerero wa kwa anthu, kapena kwa inu, kapena kwa ena, tingakhale tinali nayo mphamvu yakukulemetsani monga atumwi a Khristu.


Pakuti kudzachita ichi mwaitanidwa; pakutinso Khristu anamva zowawa m'malo mwanu, nakusiyirani chitsanzo kuti mukalondole mapazi ake;


Pakuti analandira kwa Mulungu Atate ulemu ndi ulemerero, pakumdzera Iye mau otere ochokera ku ulemerero waukulu, Uyu ndi Mwana wanga wokondedwa, amene Ine ndikondwera naye;