Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 5:11 - Buku Lopatulika

Koma iyeyu anayankha iwo, Iye amene anandichiritsa, yemweyu anati kwa ine, Yalula mphasa yako, nuyende.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma iyeyu anayankha iwo, Iye amene anandichiritsa, yemweyu anati kwa ine, Yalula mphasa yako, nuyende.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma iye adati, “Amene wandichiritsa ndiye wandiwuza kuti, ‘Nyamula mphasa yako, yenda.’ ”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma iye anayankha kuti, “Munthu amene wandichiritsa anati kwa ine, ‘Nyamula mphasa yako yamba kuyenda.’ ”

Onani mutuwo



Yohane 5:11
5 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake Ayuda ananena kwa wochiritsidwayo, Ndi Sabata, ndipo sikuloledwa kwa iwe kuyalula mphasa yako.


Anamfunsa, Munthuyo ndani wonena ndi iwe, Yalula mphasa yako, nuyende?


Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.


Ena pamenepo mwa Afarisi ananena, Munthu uyu sachokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata. Koma ena ananena, Munthu ali wochimwa akhoza bwanji kuchita zizindikiro zotere? Ndipo panali kutsutsana mwa iwo.