Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 4:8 - Buku Lopatulika

Pakuti ophunzira ake adachoka kunka kumzinda kuti akagule chakudya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti ophunzira ake adachoka kunka kumudzi kuti akagule chakudya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵiyo nkuti ophunzira ake aja atakagula chakudya mu mzinda.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

(Ophunzira ake nʼkuti atapita mʼmudzi kukagula chakudya).

Onani mutuwo



Yohane 4:8
7 Mawu Ofanana  

Koma anati kwa iwo, Muwapatse chakudya ndinu. Koma anati, Ife tilibe mikate, koma isanu yokha, ndi nsomba ziwiri zokha; kapena timuke ife kukagulira anthu awa onse zakudya.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Ndipo pamenepo anadza ophunzira ake; nazizwa kuti analinkulankhula ndi mkazi; koma panalibe wina anati, Mufuna chiyani? Kapena, mulankhula naye chiyani?


Ndipo m'mzinda muja anthu Asamariya ambiri anamkhulupirira Iye chifukwa cha mau a mkazi, wochita umboniyo, kuti, Anandiuza ine zinthu zilizonse ndinazichita.


Chifukwa chake anadza kumzinda wa Samariya, dzina lake Sikari, pafupi pa kadziko kamene Yakobo adapatsa mwana wake Yosefe;


Kunali ngati ora lachisanu ndi chimodzi. Kunadza mkazi wotuluka mu Samariya kudzatunga madzi. Yesu ananena naye, Undipatse Ine ndimwe.