Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 4:49 - Buku Lopatulika

Mkuluyo ananena kwa Iye, Ambuye, tsikani asanafe mwana wanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mkuluyo ananena kwa Iye, Ambuye, tsikani asanafe mwana wanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndunayo idati, “Ndapota nanu Ambuye, tiyeni mwana wanga asanafe.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nduna ya mfumuyo inati, “Ambuye tiyeni mwana wanga asanafe.”

Onani mutuwo



Yohane 4:49
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ine ndine wozunzika ndi waumphawi; koma Ambuye andikumbukira ine. Inu ndinu mthandizi wanga, ndi Mpulumutsi wanga, musamachedwa, Mulungu wanga.


nanena, kuti, Kamwana kanga kabuthu kalinkutsirizika; ndikupemphani Inu mufikeko, muike manja anu pa iko, kuti kapulumuke, ndi kukhala ndi moyo.


Pamenepo Yesu anati kwa iye, Ngati simuona zizindikiro ndi zozizwa, simudzakhulupirira.


Yesu ananena naye, Muka, mwana wako ali ndi moyo. Munthuyo anakhulupirira mau amene Yesu anatero naye, namuka.