Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 4:44 - Buku Lopatulika

Pakuti Yesu mwini anachita umboni kuti, Mneneri alibe ulemu m'dziko la kwao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti Yesu mwini anachita umboni kuti, Mneneri alibe ulemu m'dziko la kwao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwiniwakeyo anali atanena kuti, “Mneneri, anthu akwao samchitira ulemu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

(Tsopano Yesu mwini ananena kale kuti mneneri salandira ulemu mʼdziko lake).

Onani mutuwo



Yohane 4:44
3 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anakhumudwa chifukwa cha Iye. Koma Yesu anati kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu koma kudziko la kwao ndiko, ndi kubanja kwake.


Ndipo Yesu ananena kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu, koma m'dziko la kwao ndimo, ndi pakati pa abale ake, ndi m'nyumba yake.


Ndipo Iye anati, Indetu, ndinena kwa inu, kuti, Palibe mneneri alandirika kudziko la kwao.