Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 4:30 - Buku Lopatulika

Anatuluka iwo m'mzinda ndipo analinkudza kwa Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anatuluka iwo m'mudzi ndipo analinkudza kwa Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo anthuwo adatuluka m'mudzimo kubwera kwa Yesu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anatuluka mʼmudziwo ndi kupita kumene kunali Iye.

Onani mutuwo



Yohane 4:30
15 Mawu Ofanana  

Ndani awa amene auluka ngati mtambo, ndi monga nkhunda kumazenera ao?


Chomwecho omalizira adzakhala oyamba, ndipo oyamba adzakhala omalizira.


Tiyeni, mukaone munthu, amene anandiuza zinthu zilizonse ndinazichita: ameneyu sali Khristu nanga?


Pa mphindikati iyi ophunzira ake anampempha Iye, ndi kunena, Rabi, idyani.


Ndipo m'mzinda muja anthu Asamariya ambiri anamkhulupirira Iye chifukwa cha mau a mkazi, wochita umboniyo, kuti, Anandiuza ine zinthu zilizonse ndinazichita.


Pamenepo ndinatumiza kwa inu osachedwa; ndipo mwachita bwino mwadza kuno. Chifukwa chake taonani tilitonse pano pamaso pa Mulungu, kumva zonse Ambuye anakulamulirani.


Ndipo pakutuluka iwo anapempha kuti alankhule naonso mau awa Sabata likudzalo.


Potero, dziwani inu, kuti chipulumutso ichi cha Mulungu chitumidwa kwa amitundu; iwonso adzamva.


Ndipo lamulo linalowa moonjezera, kuti kulakwa kukachuluke; koma pamene uchimo unachuluka, pomwepo chisomo chinachuluka koposa;