Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 4:26 - Buku Lopatulika

Yesu ananena naye, Ine wakulankhula nawe ndine amene.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu ananena naye, Ine wakulankhula nawe ndine amene.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adamuuza kuti, “Ndine amene, Ineyo amene ndikulankhula nanu, mai.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Yesu anamuwuza kuti, “Amene ndikukuyankhulane, ndine amene.”

Onani mutuwo



Yohane 4:26
10 Mawu Ofanana  

Pamenepo analamulira ophunzira kuti asauze munthu kuti Iye ndiye Khristu.


Sikuloleka kwa ine kodi kuchita chimene ndifuna ndi zanga? Kapena diso lako laipa kodi chifukwa ine ndili wabwino?


Ndipo onani, alipo akuthungo amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba adzakhala akuthungo.


Kuyambira tsopano ndinena kwa inu, chisadachitike, kuti pamene chitachitika, mukakhulupirire kuti ndine amene.


Chifukwa chake ndinati kwa inu, kuti mudzafa m'machimo kwa inu, kuti mudzafa m'machimo anu, pakuti ngati simukhulupirira kuti Ine ndine, mudzafa m'machimo anu.


Chifukwa chake Yesu anati, Pamene mutadzamkweza Mwana wa Munthu, pomwepo mudzazindikira kuti Ine ndine, ndipo sindichita kanthu kwa Ine ndekha, koma monga anandiphunzitsa Atate, ndilankhula izi.