Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 4:13 - Buku Lopatulika

Yesu anayankha nati kwa iye, Yense wakumwako madzi awa adzamvanso ludzu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu anayankha nati kwa iye, Yense wakumwako madzi awa adzamvanso ludzu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adati, “Munthu aliyense womwako madzi aŵa, adzamvanso ludzu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anayankha kuti, “Aliyense amene amamwa madzi awa amamvanso ludzu,

Onani mutuwo



Yohane 4:13
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anakweza mau nati, Atate Abrahamu, mundichitire chifundo, mutume Lazaro, kuti aviike nsonga ya chala chake m'madzi, naziziritse lilime langa; pakuti ndizunzidwadi m'lawi ili la moto.


Kodi muli wamkulu ndi atate wathu Yakobo amene anatipatsa ife chitsimechi, namwamo iye yekha, ndi ana ake, ndi zoweta zake?


koma iye wakumwa madzi amene Ine ndidzampatsa sadzamva ludzu nthawi zonse; koma madzi amene Ine ndidzampatsa adzakhala mwa iye kasupe wa madzi otumphukira kumoyo wosatha.


Gwirani ntchito si chifukwa cha chakudya chimene chitayika koma cha chakudya chimene chitsalira kumoyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani inu; pakuti ameneyo Atate, ndiye Mulungu, adamlembera chizindikiro.


Makolo anu adadya m'chipululu, ndipo adamwalira.