Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 3:24 - Buku Lopatulika

Pakuti Yohane sanaikidwe m'ndende.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti Yohane sanaikidwe m'ndende.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo nkuti Yohane asanaponyedwe m'ndende.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

(Apa nʼkuti Yohane asanatsekeredwe mʼndende).

Onani mutuwo



Yohane 3:24
6 Mawu Ofanana  

Pakuti Herode adamgwira Yohane, nammanga, namuika m'nyumba yandende chifukwa cha Herodiasi, mkazi wa mbale wake Filipo.


Ndipo pamene Yesu anamva kuti anampereka Yohane, anamuka kulowa ku Galileya;


Pakuti Herode, mwini yekha, adatuma anthu namgwira Yohane, nammanga m'nyumba yandende, chifukwa cha Herodiasi, mkazi wa Filipo mbale wake; chifukwa adamkwatira iye.


Ndipo Yohane analinkubatiza mu Ainoni pafupi pa Salimu, chifukwa panali madzi ambiri pamenepo; ndipo analinkufikako anthu, nalinkubatizidwa.