Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 21:9 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene anatulukira pamtunda, anapenya moto wamakala pomwepo, ndi kansomba kosanjikikako, ndi mkate.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene anatulukira pamtunda, anapenya moto wamakala pomwepo, ndi kansomba kosanjikikako, ndi mkate.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene adafika pa mtunda, adaonapo moto wamakala, pali nsomba, ndiponso buledi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atafika pa mtunda, iwo anaona moto wamakala pamenepo ndi nsomba, ndi buledi.

Onani mutuwo



Yohane 21:9
10 Mawu Ofanana  

Pomwepo mdierekezi anamsiya Iye, ndipo onani, angelo anadza, namtumikira Iye.


ndipo ngati ndiwauza iwo amuke kwao osadya kanthu, adzakomoka panjira; ndipo ena a iwo achokera kutali.


Koma akapolo anyamata analikuimirirako, atasonkha moto wamakala; pakuti kunali kuzizira; ndipo analikuotha moto; koma Petronso anali nao alikuimirira ndi kuotha moto.


Yesu ananena nao, Tenganiko nsomba zimene mwazigwira tsopano.


Yesu anadza natenga mkate napatsa iwo, momwemonso nsomba.


Koma ophunzira ena anadza m'kangalawa, pakuti sanali kutali ndi mtunda, koma monga mikono mazana awiri, nakoka khoka la nsombazo.


Pomwepo Yesu anatenga mikateyo; ndipo pamene adayamika, anagawira iwo akukhala pansi; momwemonso ndi tinsomba, monga momwe iwo anafuna.


Pali mnyamata pano, amene ali nayo mikate isanu yabarele, ndi tinsomba tiwiri; koma nanga izi zikwanira bwanji ambiri otere?