Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 2:17 - Buku Lopatulika

Ophunzira ake anakumbukira kuti kunalembedwa, Changu cha pa nyumba yanu chandidya ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ophunzira ake anakumbukira kuti kunalembedwa, Changu cha pa nyumba yanu chandidya ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ophunzira ake adakumbukira Malembo aja akuti, “Changu chomwe ndimachitira nyumba yanu chidzandiphetsa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ophunzira ake anakumbukira kuti zinalembedwa kuti, “Kudzipereka kwanga ku nyumba yanu kudzandiphetsa.”

Onani mutuwo



Yohane 2:17
4 Mawu Ofanana  

Changu changa chinandithera, popeza akundisautsa anaiwala mau anu.


Pakuti changu cha pa nyumba yanu chandidya; ndi zotonza za iwo otonza Inu zandigwera ine.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Chifukwa chake atauka kwa akufa, ophunzira ake anakumbukira kuti ananena ichi; ndipo anakhulupirira cholemba, ndi mau amene Yesu ananena.