Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 19:8 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene Pilato anamva mau awa, anaopa koposa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene Pilato anamva mau awa, anaopa koposa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Pilato adamva mau ameneŵa, adachita mantha kwabasi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pilato atamva zimenezi, anachita mantha kwambiri,

Onani mutuwo



Yohane 19:8
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo Pilato, m'mene adamva mau awa, anatuluka ndi Yesu, nakhala pansi pa mpando woweruzira kumalo dzina lake, Bwalo lamiyala, koma mu Chihebri, Gabata.


Ayuda anamyankha iye, Tili nacho chilamulo ife, ndipo monga mwa chilamulocho ayenera kufa, chifukwa anadziyesera Mwana wa Mulungu.


Ndipo analowanso ku Pretorio, nanena kwa Yesu, Muchoka kuti? Koma Yesu sanamyankhe kanthu.