Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 18:7 - Buku Lopatulika

Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? Koma iwo anati, Yesu Mnazarayo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? Koma iwo anati, Yesu Mnazarayo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adaŵafunsanso kuti, “Mukufuna yani kodi?” Iwo aja adati “Tikufuna Yesu wa ku Nazarete.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anawafunsanso kuti, “Kodi mukumufuna ndani?” Ndipo iwo anati, “Yesu wa ku Nazareti.”

Onani mutuwo



Yohane 18:7
4 Mawu Ofanana  

nadza nakhazikika m'mzinda dzina lake Nazarete kuti chikachitidwe chonenedwa ndi aneneri kuti, Adzatchedwa Mnazarayo.


Pamenepo Yesu, podziwa zonse zilinkudza pa Iye, anatuluka, nati kwa iwo, Mufuna yani?


Ndipo m'mene anati kwa iwo, Ndine, anabwerera m'mbuyo, nagwa pansi.


Yesu anayankha, Nati, Ndine; chifukwa chake ngati mufuna Ine, lekani awa amuke;