nadza nakhazikika m'mzinda dzina lake Nazarete kuti chikachitidwe chonenedwa ndi aneneri kuti, Adzatchedwa Mnazarayo.
Yohane 18:7 - Buku Lopatulika Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? Koma iwo anati, Yesu Mnazarayo. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? Koma iwo anati, Yesu Mnazarayo. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Yesu adaŵafunsanso kuti, “Mukufuna yani kodi?” Iwo aja adati “Tikufuna Yesu wa ku Nazarete.” Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Iye anawafunsanso kuti, “Kodi mukumufuna ndani?” Ndipo iwo anati, “Yesu wa ku Nazareti.” |
nadza nakhazikika m'mzinda dzina lake Nazarete kuti chikachitidwe chonenedwa ndi aneneri kuti, Adzatchedwa Mnazarayo.