Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 18:6 - Buku Lopatulika

Ndipo m'mene anati kwa iwo, Ndine, anabwerera m'mbuyo, nagwa pansi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'mene anati kwa iwo, Ndine, anabwerera m'mbuyo, nagwa pansi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Yesu adaŵayankha kuti, “Ndine, ndilipo,” iwo adabwerera m'mbuyo nagwa pansi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Yesu anati, “Ndine,” iwo anabwerera mʼmbuyo ndi kugwa pansi.

Onani mutuwo



Yohane 18:6
9 Mawu Ofanana  

Achite manyazi nabwerere m'mbuyo. Onse akudana naye Ziyoni.


Pondifika ine ochita zoipa kudzadya mnofu wanga, inde akundisautsa ndi adani anga, anakhumudwa iwo nagwa.


Achite manyazi nadodome iwo akulondola moyo wanga kuti auononge. Abwerere m'mbuyo, nachite manyazi iwo okondwera kundichitira choipa.


Anayankha Iye, Yesu Mnazarayo. Yesu ananena nao, Ndine. Koma Yudasi yemwe, wompereka Iye, anaima nao pamodzi.


Pamenepo anawafunsanso, Mufuna yani? Koma iwo anati, Yesu Mnazarayo.