Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 17:7 - Buku Lopatulika

Azindikira tsopano kuti zinthu zilizonse zimene mwandipatsa Ine zichokera kwa Inu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Azindikira tsopano kuti zinthu zilizonse zimene mwandipatsa Ine zichokera kwa Inu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsopano akudziŵa kuti zonse zimene mudandipatsa nzochokera kwa Inu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsopano akudziwa kuti zonse zimene munandipatsa nʼzochokera kwa Inu.

Onani mutuwo



Yohane 17:7
11 Mawu Ofanana  

Tsiku lomwelo mudzazindikira kuti ndili Ine mwa Atate wanga, ndi inu mwa Ine, ndi Ine mwa inu.


Zinthu zilizonse Atate ali nazo ndi zanga; chifukwa chake ndinati, kuti atenga za mwa Ine, nadzalalikira kwa inu.


chifukwa ali anu: ndipo zanga zonse zili zanu, ndi zanu zili zanga; ndipo ndilemekezedwa mwa iwo.


Ndalionetsera dzina lanu kwa anthu amene mwandipatsa Ine m'dziko lapansi; anali anu, ndipo mwandipatsa Ine iwo; ndipo adasunga mau anu.


chifukwa mau amene munandipatsa Ine ndinapatsa iwo; ndipo analandira, nazindikira koona kuti ndinatuluka kwa Inu, ndipo anakhulupirira kuti Inu munandituma Ine.


Chifukwa chake Yesu anati, Pamene mutadzamkweza Mwana wa Munthu, pomwepo mudzazindikira kuti Ine ndine, ndipo sindichita kanthu kwa Ine ndekha, koma monga anandiphunzitsa Atate, ndilankhula izi.