Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 17:16 - Buku Lopatulika

Siali a dziko lapansi monga Ine sindili wa dziko lapansi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Siali a dziko lapansi monga Ine sindili wa dziko lapansi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo sali a dziko lapansi, monga Inenso sindili wa dziko lapansi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo si a dziko lapansi, monga Ine sindilinso wa dziko lapansi.

Onani mutuwo



Yohane 17:16
3 Mawu Ofanana  

Ine ndawapatsa iwo mau anu; ndipo dziko lapansi, linadana nao, chifukwa sakhala a dziko lapansi, monga Ine sindikhala wa dziko lapansi.


Ndipo ananena nao, Inu ndinu ochokera pansi; Ine ndine wochokera Kumwamba; inu ndinu a dziko lino lapansi; sindili Ine wa dziko lino lapansi.


mwa ichi alankhula monga ochokera m'dziko lapansi, ndipo dziko lapansi liwamvera.