Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 16:9 - Buku Lopatulika

za machimo, chifukwa sakhulupirira Ine;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

za machimo, chifukwa sakhulupirira Ine;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ngolakwa pa za kuchimwa, chifukwa sandikhulupirira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Za uchimo, chifukwa anthu sakhulupirira Ine.

Onani mutuwo



Yohane 16:9
18 Mawu Ofanana  

Amene akhulupirira nabatizidwa, adzapulumutsidwa; koma amene sakhulupirira adzalangidwa.


Ndipo atadza Iyeyo, adzatsutsa dziko lapansi za machimo, ndi za chilungamo, ndi za chiweruziro;


Ndipo kale ine ndinali wamoyo popanda lamulo; koma pamene lamulo linadza, uchimo unatsitsimuka, ndipo ine ndinafa.


ndingakhale kale ndinali wamwano, ndi wolondalonda, ndi wachipongwe; komatu anandichitira chifundo, popeza ndinazichita wosazindikira, wosakhulupirira;


Tapenyani, abale, kuti kapena ukakhale mwa wina wa inu mtima woipa wosakhulupirira, wakulekana ndi Mulungu wamoyo;