Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 16:6 - Buku Lopatulika

Koma chifukwa ndalankhula izi ndi inu chisoni chadzala mumtima mwanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma chifukwa ndalankhula izi ndi inu chisoni chadzala mumtima mwanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'mitima mwanu mwadzaza chisoni chifukwa ndakuuzani zimenezi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Muli ndi chisoni kwambiri chifukwa ndakuwuzani zimene.

Onani mutuwo



Yohane 16:6
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene ananyamuka pakupemphera anadza kwa ophunzira, nawapeza ali m'tulo ndi chisoni,


Ndipo anati kwa iwo, Mau awa ndi otani mulandizanawo poyendayenda? Ndipo anaima ndi nkhope zao zachisoni.


Mtima wanu usavutike; mukhulupirira Mulungu, khulupirirani Inenso.