Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 16:1 - Buku Lopatulika

Izi ndalankhula ndi inu kuti mungakhumudwitsidwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Izi ndalankhula ndi inu kuti mungakhumudwitsidwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Ndakuuziranitu zonsezi kuti mungadzataye mtima.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ine ndakuwuzani zonsezi kuti musadzakhumudwe.

Onani mutuwo



Yohane 16:1
11 Mawu Ofanana  

Ndipo wodala iye amene sakhumudwa chifukwa cha Ine.


ndipo alibe mizu mwa iye, koma akhala nthawi yaing'ono; ndipo pakudza nsautso kapena zunzo chifukwa cha mau, iye akhumudwa pomwepo.


Ndipo iwo anakhumudwa chifukwa cha Iye. Koma Yesu anati kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu koma kudziko la kwao ndiko, ndi kubanja kwake.


Ndipo pomwepo ambiri adzakhumudwa, nadzaperekana wina ndi mnzake, nadzadana wina ndi mnzake.


Izi ndalankhula ndi inu, kuti chimwemwe changa chikhale mwa inu, ndi kuti chimwemwe chanu chidzale.


Koma zinthu izi ndalankhula ndi inu kuti ikadza nthawi yao, mukakumbukire kuti ndinakuuzani. Koma izi sindinanene kwa inu kuyambira pachiyambi, chifukwa ndinali pamodzi ndi inu.


Kuli kwabwino kusadya nyama, kapena kusamwa vinyo, kapena kusachita chinthu chilichonse chakukhumudwitsa mbale wako.


kuti mukayese inu zinthu zosiyana; kuti mukakhale a mtima woona ndi wosalakwa, kufikira tsiku la Khristu;


Ndipo, Mwala wakukhumudwa nao, ndi thanthwe lophunthwitsa. Kwa iwo akukhumudwa ndi mau, pokhala osamvera, kumenekonso adaikidwako.